Back to Languages

    Chichewa - Chapter 104

    Translation by Al Haji Yusuf Muhammad Kanyamula

    Verse 1

    Tsoka kwa aliyense amene amajeda ndi kuononga mbiri ya anzake

    Verse 2

    Amene amasonkhanitsa chuma chake ndi kumachiwerenga

    Verse 3

    Iye amaganiza kuti chuma chake chidzamuchititsa iye kukhala ndi moyo wamuyaya

    Verse 4

    Iyayi! Ndithudi iye adzaponyedwa ku moto woononga

    Verse 5

    Kodi chidzakuuza kuti moto woononga ndi chiyani

    Verse 6

    Ndi moto wa Mulungu umene Mwini wake anauyatsa

    Verse 7

    Umene umafuka m’mitima ya anthu

    Verse 8

    Ndithudi udzawatsekereza mbali iliyonse

    Verse 9

    M’sanamila zoima